Proverbs 3:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, usanyoze malango a Chauta, usatope nako kudzudzula kwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, usapeputse mwambo wa Yehova, ngakhale kutopa ndi kudzudzula kwake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga usanyoze malangizo a Yehova, ndipo usayipidwe ndi chidzudzulo chake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, usapeputse mwambo wa Yehova, Ngakhale kutopa ndi kudzudzula kwace;