Proverbs 3:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Chauta amadzudzula yemwe amamkonda, monga momwe atate amamchitira mwana wokondwera naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti Yehova adzudzula omwe awakonda; monga atate mwana amene akondwera naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paja Yehova amadzudzula amene amamukonda, monga abambo achitira mwana amene amakondwera naye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova adzudzula omwe awakonda; Monga atate mwana amene akondwera naye.