Proverbs 3:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nzeru ili ngati mtengo woŵapatsa moyo oigwiritsa. Ngodala amene amaikangamira molimbika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndiyo mtengo wa moyo wa akuigwira; wakuiumirira ngwodala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nzeru ili ngati mtengo wopatsa moyo kwa oyigwiritsitsa; wodala munthu amene amayigwiritsa kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiyo mtengo wa moyo wa akuigwira; Wakulumirira ngwodala.