Proverbs 3:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adakhazikitsa dziko lapansi, Chauta adaonetsa nzeru. Pamene adakhazikitsa zakumwamba, adaonetsa nzeru za kumvetsa bwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova anakhazika dziko ndi nzeru; naika zamwamba ndi luntha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru. Anagwiritsanso ntchito nzeru zakudziwa bwino zinthu pamene ankakhazikitsa zakumwamba.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova anakhazika dziko ndi nzeru; Naika zamwamba ndi luntha.