Proverbs 3:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka, ndipo udzakhala ndi moyo wabwino kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti adzakuonjezera masiku ambiri, ndi zaka za moyo ndi mtendere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka ndipo udzakhala pa mtendere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti adzakuonjezera masiku ambiri, Ndi zaka za moyo ndi mtendere.