Proverbs 3:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene adatumphutsa madzi kuchoka kunsi kwa dziko, ndipo mitambo idagwetsa mvula, adaonetsa nzeru zodziŵa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zakuya zinang'ambika ndi kudziwa kwake; thambo ligwetsa mame.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwa nzeru zake Yehova anatumphutsa madzi kuchokera mʼnthaka ndiponso mitambo inagwetsa mvula.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zakuya zinang'ambika ndi kudziwakwace; Thambo ligwetsa mame.