Proverbs 3:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, usunge nzeru yeniyeni usunge mkhalidwe wa kulingalira bwino, ziŵiri zimenezi zisakuthaŵe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, zisachokere kumaso ako; sunga nzeru yeniyeni ndi kulingalira;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga usunge nzeru yeniyeni ndi khalidwe lomalingarira zinthu bwino. Zimenezi zisakuchokere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, zisacokere ku maso ako; Sunga nzeru yeniyeni ndi kulingalira;