Proverbs 3:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usamakangane ndi munthu popanda chifukwa pamene iyeyo sadakuchite choipa chilichonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usakangane ndi munthu chabe, ngati sanakuchitire choipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usakangane ndi munthu wopanda chifukwa pamene iye sanakuchitire zoyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usakangane ndi munthu cabe, Ngati sanakucitira coipa,