Proverbs 3:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja Chauta amanyansidwa ndi munthu woipa, koma olungama okha amayanjana nawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti wamphulupulu anyansa Yehova; koma chinsinsi chake chili ndi oongoka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa koma amayanjana nawo anthu olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti wamphulupulu anyansa Yehova; Koma cinsinsi cace ciri ndi oongoka.