Proverbs 30:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati wakhala ukupusa ndi kumadzikweza, kapena wakhala ukukonzekera kuchita zoipa, yamba wati chete, uziganize bwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati wapusa podzikweza, ngakhale kuganizira zoipa, tagwira pakamwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngati wakhala ukupusa ndi kumadzikweza wekha, kapena ngati wakhala ukukonzekera zoyipa, ndiye khala kaye chete, uganizire bwino!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati wapusa podzikweza, Ngakhale kuganizira zoipa, tagwira pakamwa.