Proverbs 4:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwo ajatu sangagone, mpaka atachita ndithu choipa. Tulo sangatiwone, mpaka atakhumudwitsapo munthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti akapanda kuchita zoipa, samagona; ndipo akapanda kukhumudwitsa wina, tulo tao tiwachokera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti iwo sagona mpaka atachita zoyipa; tulo salipeza mpaka atapunthwitsa munthu wina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti akapanda kucita zoipa, samagona; Ndipo akapanda kukhumudwitsa wina, tulo tao tiwacokera.