Proverbs 4:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja kuchita zoipa ndiye chakudya chao, kuchita ndeu ndiye chakumwa chao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti amadya chakudya cha uchimo, namwa vinyo wa chifwamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paja chakudya chawo ndicho kuchita zoyipa basi ndipo chakumwa chawo ndi chiwawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti amadya cakudya ca ucimo, Namwa vinyo wa cifwamba.