Proverbs 4:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Njira ya anthu oipa ili ngati mdima wandiweyani. Satha kuzindikira kuti aphunthwa pa chiyani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira ya oipa ikunga mdima; sadziwa chimene chiwaphunthwitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma njira ya anthu oyipa ili ngati mdima wandiweyani; iwo sadziwa chomwe chimawapunthwitsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira ya oipa ikunga mdima; Sadziwa cimene ciwapunthwitsa,