Proverbs 4:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, mvetsetsa mau anga. Tchera khutu ku zimene ndikunena.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, tamvera mau anga; tcherera makutu ku zonena zanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga, mvetsetsa zimene ndikunena; tchera khutu ku mawu anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, tamvera mau anga; Cherera makutu ku zonena zanga.