Proverbs 4:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene ndinali mwana m'nyumba mwa atate anga, m'menemo ndili kamwana kapamtima ka amai anga,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ndinali mwana kwa atate wanga, wokondedwa ndi mai, ndine ndekha, sanabale wina.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga; mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ndinali mwana kwa atate wanga, Wokondedwa ndi mai, ndine ndekha, sanabala wina.