Proverbs 4:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usaiŵale mau a pakamwa pangaŵa, usatayane nawo, Ukhale ndi nzeru, ndiponso khalidwe la kumvetsa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tenga nzeru, tenga luntha; usaiwale, usapatuke pa mau a m'kamwa mwanga;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu; usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tenga nzeru, tenga luntha; Usaiwale, usapatuke pa mau a m'kamwa mwanga;