Proverbs 4:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chachikulu pa nzeru ndi ichi: Kaya nchiyani chimene ungapate, peza nzeruyo, usalephere kupata khalidwe la kumvetsa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nzeru ipambana, tatenga nzeru; m'kutenga kwako konseko utenge luntha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru. Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nzeru ipambana, tatenga nzeru; M'kutenga kwako konseko utenge luntha.