Proverbs 5:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pang'onong'ono, bwenzi nditaonongekeratu pakati pa mpingo wonse utasonkhana.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikadakhala m'zoipa zonse, m'kati mwa msonkhano ndi khamu la anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndatsala pangʼono kuti ndiwonongeke pakati pa msonkhano wonse.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikadakhala m'zoipa zonse, M'kati mwa msonkhano ndi khamu la anthu.