Proverbs 5:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Uzikhutira ndi mkazi wako, uzikondwa ndi mkazi wa unyamata wako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adalitsike kasupe wako; ukondwere ndi mkazi wokula nayo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova adalitse kasupe wako, ndipo usangalale ndi mkazi wa unyamata wako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adalitsike kasupe wako; Ukondwere ndi mkazi wokula nayo.