Proverbs 5:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Uzilambalala kutali ndi mkazi wotere, usamafika kufupi ndi khomo la nyumba yake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Siyanitsa njira yako kutali kwa iyeyo, osayandikira ku khomo la nyumba yake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uziyenda kutali ndi mkazi wotereyo, usayandikire khomo la nyumba yake,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Siyanitsa njira yako kutari kwa iyeyo, Osayandikira ku khomo la nyumba yace;