Proverbs 6:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi udakodwa ndi mau a pakamwa pako pomwe, kodi udagwidwa ndi mau olankhula iwe wemwe?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wakodwa ndi mau a m'kamwa mwako, wagwidwa ndi mau a m'kamwa mwako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ngati wagwidwa ndi zimene iwe unanena, wakodwa ndi mawu a mʼkamwa mwako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wakodwa ndi mau a m'kamwa mwako, Wagwidwa ndi mau a m'kamwa mwako.