Proverbs 7:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, mvera mau anga, malamulo anga akhale chuma chako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, sunga mau anga, ukundike malangizo anga,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga, mvera mawu anga; usunge bwino malamulo angawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, sunga mau anga, Ukundike malangizo anga;