Proverbs 7:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye mkazi adadzakumana naye, atavala ngati mkazi wadama, wa mtima wonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo taona, mkaziyo anamchingamira, atavala zadama wochenjera mtima,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo mkaziyo anadzakumana naye, atavala ngati munthu wachiwerewere wa mtima wonyenga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo taona, mkaziyo anamcingamira, Atabvala zadama wocenjera mtima,