Proverbs 7:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mkaziyo ndi wosakhazikika ndi wopanda manyazi, kamwendom'njira wosakhala pakhomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ali wolongolola ndi wosaweruzika, mapazi ake samakhala m'nyumba mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve, iye ndi wosakhazikika pa khomo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ali wolongolola ndi wosaweruzika, Mapazi ace samakhala m'nyumba mwace.