Proverbs 7:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwina umpeza pa mseu, mwina pa msika, amachita kukhalizira munthu pa mphambano iliyonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwina ali kumakwalala, mwina ali kumabwalo, nabisalira pa mphambano zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika, ndipo amadikirira munthu pa mphambano iliyonse).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwina ali kumakwalala, mwina ali kumabwalo, Nabisalira pa mphambano zonse.