Proverbs 7:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pomweponso ndawazapo zonunkhira za mure, ndi mankhwala a fungo lokoma a aloyi, ndi a sinamoni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndakapiza pamphasa panga mankhwala onunkhira a mure ndi chisiyo ndi sinamoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira za mure, mafuta onunkhira a aloe ndi sinamoni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndakapiza pamphasa panga mankhwala onunkhira A mvunja ndi cisiyo ndi mtanthanyerere.