Proverbs 7:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwamuna wanga kulibe, ali pa ulendo wautali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti mwamuna kulibe kwathu, wapita ulendo wa kutali;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako; wapita ulendo wautali:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti mwamuna kulibe kwathu, Wapita ulendo wa kutari;