Proverbs 7:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Utsate malamulo anga, ndipo udzakhala ndi moyo. Usamale malangizo anga monga umachitira ndi maso ako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sunga malangizo anga, nukhale ndi moyo; ndi malamulo anga ngati mwana wa diso lako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo; samala malangizo angawa monga uchitira ndi maso ako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sunga malangizo anga, nukhale ndi moyo; Ndi malamulo anga ngati mwana wa diso lako.