Proverbs 7:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amamkopa mnyamatayo ndi mau onyengerera, amamkakamiza ndi mau ake oshashalika.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amkakamiza ndi kukoka kwa mau ake, ampatutsa ndi kusyasyalika kwa milomo yake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo; amukopa ndi mawu ake oshashalika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amkakamiza ndi kukoka kwa mau ace, Ampatutsa ndi kusyasyalika kwa milomo yace.