Proverbs 7:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo mnyamatayo amatsatira mkaziyo monga momwe ng'ombe imapitira kokaphedwa, kapena monga momwe mbaŵala imakodwera mu msampha,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mnyamatayo amtsata posachedwa, monga ng'ombe ipita kukaphedwa; ndi monga unyolo umadza kulanga chitsiru;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo ngati ngʼombe yopita kukaphedwa, monga momwe mbawala ikodwera mu msampha,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mnyamatayo amtsata posacedwa, monga ng'ombe ipita kukaphedwa; Ndi monga unyolo umadza kulanga citsiru;