Proverbs 7:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mpaka muvi kuilasa m'mimba mwake. Amakhala ngati mbalame yothamangira m'khwekhwe, osadziŵako kuti aferapo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mpaka muvi ukapyoza mphafa yake; amtsata monga mbalame yothamangira msampha; osadziwa kuti adzaononga moyo wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mpaka muvi utalasa chiwindi chake, chimakhala ngati mbalame yothamangira mʼkhwekhwe, osadziwa kuti moyo wake uwonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mpaka mubvi ukapyoza mphafa yace; Amtsata monga mbalame yotamangira msampha; Osadziwa kuti adzaononga moyo wace.