Proverbs 7:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Achite ngati waŵamangirira ku chala, ngati waŵadinda mumtima mwako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Uwamange pa zala zako, uwalembe pamtima pako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uchite ngati wawamangirira pa zala zako, ndiponso ngati kuti wawalemba pa mtima pako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Uwamange pa zala zako, Uwalembe pamtima pako;