Proverbs 7:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nzeru uiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe la kumvetsa zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongo wanga; nutche luntha mbale wako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,” ndipo khalidwe lomvetsa bwino zinthu ulitchule kuti, “Bwenzi langa lapamtima.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nena kwa nzeru, Ndiwe mlongwanga; Nuche luntha mbale wako.