Proverbs 7:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ankayenda m'njira pafupi ndi nyumba ya mkaziyo, ankaphera mu mseu wa kunyumba kumeneko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
alikupita pakhwalala pafupi ndi mphambano ya pa mkaziyo, ndi kuyenda pa njira ya kunyumba yake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo, kuyenda molunjika nyumba ya mkaziyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Alikupita pakhwalala pafupi ndi mphambano ya pa mkaziyo, Ndi kuyenda pa njira ya ku nyumba yace;