Proverbs 7:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inali nthaŵi ya chisisira, madzulo, nthaŵi yausiku, kuli mdima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pa madzulo kuli sisiro, pakati pa usiku pali mdima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inali nthawi yachisisira madzulo, nthawi ya usiku, kuli mdima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pa madzulo kuli sisiro, Pakati pa usiku pali mdima,