Proverbs 8:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa panga palankhula zoona, kulankhula zoipa nchinthu chonyansa m'kamwa mwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti m'kamwa mwanga mudzalankhula ntheradi, zoipa zinyansa milomo yanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakamwa panga pamayankhula zoona ndimanyansidwa ndi kuyankhula zoyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti m'kamwa mwanga mudzalankhula ntheradi, Zoipa zinyansa milomo yanga.