Proverbs 9:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Leka kupulukira kwako, kuti ukhale ndi moyo, uziyenda m'njira ya nzeru.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lekani, achibwana inu, nimukhale ndi moyo; nimuyende m'njira ya nzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo; yendani njira ya nzeru yomvetsa zinthu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lekani, acibwana inu, nimukhale ndi moyo; Nimuyende m'njira ya nzeru.