Psalms 105:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adati, “Ndidzakupatsa dziko la Kanani kuti likhale choloŵa chako chokhalira iweyo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi kunena kuti, Ndidzakupatsa iwe dziko la Kanani, gawo la cholandira chako;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndidzapereka kwa iwe dziko la Kanaani ngati gawo la cholowa chako.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi kunena kuti, Ndidzakupatsa iwe dziko la Kanani, Gawo la colandira cako;