Psalms 105:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
sadalole ndi mmodzi yemwe kuti aŵapsinje, adalanga mafumu ena chifukwa cha anthu akewo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sanalola munthu awasautse; ndipo anadzudzula mafumu chifukwa cha iwowa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye sanalole wina aliyense kuwapondereza; anadzudzula mafumu chifukwa cha iwo:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sanalola munthu awasautse; Ndipo anadzudzula mafumu cifukwa ca iwowa;