Psalms 107:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Athokoze Chauta chifukwa cha chikondi chake chosasinthika, chifukwa cha ntchito zake zodabwitsa kwa anthu onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ayamike Yehova chifukwa cha chifundo chake, ndi zodabwitsa zake za kwa ana a anthu!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha ndi chifukwa cha machitidwe ake odabwitsa kwa anthu onse,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ayamike Yehova cifukwa ca cifundo cace, Ndi zodabwiza zace za kwa ana a anthu!