Psalms 112:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amene amakongoza mosafuna phindu, amene amayendetsa ntchito zake mwachilungamo, zinthu zimamuyendera bwino.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wodala munthu wakuchitira chifundo, nakongoletsa; adzalimbika nao mlandu wake poweruzidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wodala munthu wakudtira cifundo, nakongoletsa; Adzalimbika nao mlandu wace poweruzidwa.