Psalms 112:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Saopa akamva zoipa zimene zachitika. Mtima wake ndi wosasinthika, amakhulupirira Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sadzaopa mbiri yoipa; mtima wake ngwokhazika, wokhulupirira Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Saopa akamva zoyipa zimene zachitika; mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sadzaopa mbiri yoipa; Mtima wace ngwokhazikika, wakhulupirira Yehova.