Psalms 113:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndani angalingane ndi Chauta, Mulungu wathu, amene akukhala kumwamba,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akunga Yehova Mulungu wathu ndani? Amene akhala pamwamba patali,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu, Iye amene amakhala mwaufumu mmwamba?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akunga Yehova Mulungu wathu ndani? Amene akhala pamwamba patali,