Psalms 115:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa chiyani mitundu ina ya anthu iziti, “Mulungu wao ali kuti?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aneneranji amitundu, Ali kuti Mulungu wao?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti, “Mulungu wawo ali kuti?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aneneranji amitundu, Ali kuti Mulungu wao?