Psalms 116:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta ndi wokoma mtima ndi wolungama. Mulungu wathu ndi wachifundo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova ngwa chifundo ndi wolungama; ndi Mulungu wathu ngwa nsoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova ngwa cifundo ndi wolungama; Ndi Mulungu wathu ngwa nsoni.