Psalms 118:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
dzanja lamanja la Chauta lapambana, dzanja lamanja la Chauta limagonjetsa mwamphamvu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Dzanja lamanja la Yehova likwezeka, Dzanja lamanja la Yehova lichita mwamphamvu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Dzanja lamanja la Yehova licita mwamphamvu.