Psalms 119:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse, musalole kuti ndisiye kumvera malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinakufunani ndi mtima wanga wonse; ndisasokere kusiyana nao malamulo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse; musalole kuti ndisochere kuchoka pa malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinakufunani ndi mtima wanga wonse; Ndisasokere kusiyana nao malamulo anu.