Psalms 119:100 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndili ndi nzeru kupambana okalamba, pakuti ndimatsata malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndizindikira koposa okalamba popeza ndinasunga malangizo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndili ndi nzeru zochuluka zomvetsera zinthu kuposa anthu okalamba, popeza ndimamvera malangizo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndizindikira koposa okalamba Popeza ndinasunga malangizo anu.