Psalms 119:101 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimaletsa miyendo yanga kuti isayende m'njira yoipa iliyonse, kuti choncho ndizisunga mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinaletsa mapazi anga njira iliyonse yaoipa, kuti ndisamalire mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimaletsa miyendo yanga kuyenda mʼnjira iliyonse yoyipa kuti ndithe kumvera mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinaletsa mapazi anga njira iri yonse yoipa, Kuti ndisamalire mau anu.