Psalms 119:103 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
mau anu ndi otsekemera kwambiri ndikaŵalaŵa. Amatsekemera kuposa uchi m'kamwa mwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau anu azunadi powalawa ine! Koposa uchi m'kamwa mwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu anu ndi otsekemera ndikawalawa, otsekemera kuposa uchi mʼkamwa mwanga!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau anu azunadi powalawa ine! Koposa uci m'kamwa mwanga.